Eksodo 14:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Aejipito anawalondola, nalowa pakati pa nyanja powatsata, ndiwo akavalo onse a Farao, magaleta ake, ndi apakavalo ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Aejipito anawalondola, nalowa pakati pa nyanja powatsata, ndiwo akavalo onse a Farao, magaleta ake, ndi apakavalo ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Aejipito aja adalondola Aisraelewo mpaka kukaloŵa nawo m'nyanja muja. Akavalo onse a Farao adaloŵa m'nyanja, pamodzi ndi magaleta ake ndi oŵayendetsa ake omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Aigupto onse, Farao, ndi onse okwera pa magaleta ndi akavalo anawalondola ndipo analowa mʼmadzi. Onani mutuwo |