Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 13:4 - Buku Lopatulika

4 Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mukuchoka ku Ejipito pa tsiku lalero, mwezi uno wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Pa tsiku la lero mwezi uno wa Abibu, mukutuluka mʼdziko la Igupto.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 13:4
6 Mawu Ofanana  

Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe.


Mwezi uno uzikhala kwa inu woyamba wa miyezi; muziuyesa mwezi woyamba wa chaka.


Uzisunga chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa; masiku asanu ndi awiri uzidya mkate wopanda chotupitsa, monga ndinakuuza, nyengo yoikika, mwezi wa Abibu, pakuti m'menemo unatuluka mu Ejipito; koma asaoneke munthu pamaso panga opanda kanthu;


Uzisunga chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa. Uzidya mkate wopanda chotupitsa masiku asanu ndi awiri, monga ndakuuza pa nthawi yonenedwa, m'mwezi wa Abibu; pakuti mwezi wa Abibu unatuluka mu Ejipito.


Ndipo ndinakhazikitsanso nao chipangano changa, kuwapatsa dziko la Kanani, dziko la maulendo ao, anali alendo m'mwemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa