Eksodo 13:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo chizikhala ngati chizindikiro padzanja lako, ndi chapamphumi pakati pamaso ako; pakuti Yehova anatitulutsa mu Ejipito ndi dzanja lamphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo chizikhala ngati chizindikiro pa dzanja lako, ndi chapamphumi pakati pa maso ako; pakuti Yehova anatitulutsa m'Ejipito ndi dzanja lamphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chimenechi chidzakhala chikumbutso, monga ngati chizindikiro chomangidwa pa dzanja lanu kapena pamphumi panu, chifukwa Chauta adatitulutsa ku Ejipito ndi dzanja lake lamphamvu.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo chidzakhala kwa inu ngati chizindikiro chomangidwa pa dzanja lanu ndi pamphumi panu kuonetsa kuti Yehova anakutulutsani mʼdziko la Igupto ndi dzanja lake lamphamvu.” Onani mutuwo |