Eksodo 12:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo kunakhala pakutha zaka mazana anai kudza makumi atatu, inde panakhala tsiku lomwelo, makamu onse a Yehova anatuluka m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo kunakhala pakutha zaka mazana anai kudza makumi atatu, inde panakhala tsiku lomwelo, makamu onse a Yehova anatuluka m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Pa tsiku lomwe zaka 430 zinkatha, magulu onse a Chauta adachokako ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Pa tsiku lomwelo limene anakwanitsa zaka 430, magulu onse a Yehova anatuluka mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |