Eksodo 12:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo kukhala kwa ana a Israele anakhala mu Ejipito ndiko zaka mazana anai kudza makumi atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo kukhala kwa ana a Israele anakhala m'Ejipito ndiko zaka mazana anai kudza makumi atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Aisraele adakhalako zaka 430 ku Ejipito kuja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Ndipo Aisraeli anakhala ku Igupto kwa zaka 430. Onani mutuwo |