Eksodo 10:27 - Buku Lopatulika27 Koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo anakana kuwaleka amuke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo anakana kuwaleka amuke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma Chauta adaumitsa Farao mtima, ndipo sadalole kuti anthuwo apite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao ndipo sanafune kuwalola kuti apite. Onani mutuwo |