Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 10:27 - Buku Lopatulika

27 Koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo anakana kuwaleka amuke.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo anakana kuwaleka amuke.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Koma Chauta adaumitsa Farao mtima, ndipo sadalole kuti anthuwo apite.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao ndipo sanafune kuwalola kuti apite.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 10:27
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao; pakuti ndaumitsa mtima wake, ndi mtima wa anyamata ake, kuti ndiike zizindikiro zanga izi pakati pao;


Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole ana a Israele amuke.


Ndipo Mose ndi Aroni anachita zozizwa izi zonse pamaso pa Farao; koma Yehova analimbitsa mtima wake wa Farao, ndipo sanalole ana a Israele atuluke m'dziko lake.


Ndipo ndidzalimbitsa mtima wake wa Farao kuti awalondole; ndipo ndidzalemekezedwa pa Farao ndi pa nkhondo yake yonse; pamenepo Aejipito adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndipo anachita chomwecho.


Ndipo Yehova analimbitsa mtima wa Farao, mfumu ya Aejipito, ndipo iye analondola ana a Israele; koma ana a Israele adatuluka ndi dzanja lokwezeka.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Pakumuka iwe kubwerera kunka ku Ejipito, usamalire uchite zozizwa zonse ndaziika m'dzanja lako, pamaso pa Farao; koma Ine ndidzalimbitsa mtima wake kuti asadzalole anthu kupita.


Chotero Iye achitira chifundo amene Iye afuna, ndipo amene Iye afuna amuumitsa mtima.


Ndipo otsala a anthu osaphedwa nayo miliri iyo sanalape ntchito ya manja ao, kuti asapembedzere ziwanda, ndi mafano agolide, ndi asiliva, ndi amkuwa, ndi a mwala, ndi amtengo, amene sangathe kupenya, kapena kumva, kapena kuyenda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa