Eksodo 10:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mose adachoka kwa Farao kuja, nakapemphera kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mose anachoka kwa Farao nakapemphera kwa Yehova. Onani mutuwo |