Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 10:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mose adachoka kwa Farao kuja, nakapemphera kwa Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mose anachoka kwa Farao nakapemphera kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 10:18
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anabweza mphepo yolimbatu ya kumadzulo, imene inapita nalo dzombe niliponya mu Nyanja Yofiira: silinatsale dzombe limodzi pakati pa malire onse a Ejipito.


Ndipo Mose ndi Aroni anatuluka kwa Farao; ndi Mose anafuulira kwa Yehova kunena za achule amene adawaika pa Farao.


Pamenepo Farao anaitana Mose ndi Aroni, nati, Mundipembere Yehova, kuti andichotsere ine ndi anthu anga achulewo; ndipo ndidzalola anthu amuke, kuti amphere Yehova nsembe.


Koma Mose anati kwa Farao, Ulemu ndi wanu, wa ine ai; ndipembere inu ndi anyamata anu ndi anthu anu liti, kuti aonongeke achulewo, achokere inu ndi nyumba zanu, atsale m'mtsinje mokha?


Pamenepo anthu anafuulira kwa Mose; ndi Mose anapemphera kwa Yehova, ndi motowo unazima.


koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu;


dalitsani iwo akutemberera inu, pemphererani iwo akuchitira inu chipongwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa