Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 1:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo anafa Yosefe, ndi abale ake onse, ndi mbadwo uwo wonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo anafa Yosefe, ndi abale ake onse, ndi mbadwo uwo wonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono Yosefe adamwalira, abale ake ndi mbadwo wao wonse uja adamwaliranso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Tsono Yosefe ndi abale ake onse ndiponso mʼbado wawo wonse anamwalira.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 1:6
5 Mawu Ofanana  

Yosefe ndipo anati kwa abale ake, Ndilinkufa ine, koma Mulungu adzaonekera kwa inu, adzakuchotsani inu m'dziko muno kubwera kunka ku dziko limene analumbirira kwa Abrahamu ndi kwa Isaki, ndi kwa Yakobo.


Ndipo anafa Yosefe, anali wa zaka zana limodzi ndi khumi; ndipo anakonza thupi lake ndi mankhwala osungira, ndipo anamuika iye m'bokosi mu Ejipito.


Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.


Ndiponso mbadwo uwu wonse unasonkhanidwa kuikidwa kwa makolo ao; nuuka mbadwo wina pambuyo pao; wosadziwa Yehova kapena ntchitoyi adaichitira Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa