Eksodo 1:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo mfumu ya Aejipito inanena ndi anamwino a Ahebri, dzina lake la wina ndiye Sifira, dzina la mnzake ndiye Puwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo mfumu ya Aejipito inanena ndi anamwino a Ahebri, dzina lake la wina ndiye Sifira, dzina la mnzake ndiye Puwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono mfumu ya ku Ejipito ija idaitana azamba amene ankathandiza azimai achihebri pochira. Wina mwa azamba ameneŵa anali Sifira, wina anali Puwa. Mfumuyo idauza azambawo kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mfumu ya Igupto inati kwa azamba a Chihebri omwe mayina awo anali Sifira ndi Puwa, Onani mutuwo |