Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 1:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo mfumu ya Aejipito inanena ndi anamwino a Ahebri, dzina lake la wina ndiye Sifira, dzina la mnzake ndiye Puwa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo mfumu ya Aejipito inanena ndi anamwino a Ahebri, dzina lake la wina ndiye Sifira, dzina la mnzake ndiye Puwa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono mfumu ya ku Ejipito ija idaitana azamba amene ankathandiza azimai achihebri pochira. Wina mwa azamba ameneŵa anali Sifira, wina anali Puwa. Mfumuyo idauza azambawo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mfumu ya Igupto inati kwa azamba a Chihebri omwe mayina awo anali Sifira ndi Puwa,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 1:15
4 Mawu Ofanana  

nawawitsa moyo wao ndi ntchito yolimba, ya dothi ndi ya njerwa, ndi ntchito zonse za pabwalo, ntchito zao zonse zimene anawagwiritsa nzosautsa.


ninati, Pamene muchiza akazi a Ahebri nimuwaone pamipando; akakhala mwana wamwamuna, mumuphe; akakhala wamkazi, akhale ndi moyo.


Ndipo ananena nao, Ndine Muhebri, ndiopa Yehova Mulungu wa Kumwamba, amene analenga nyanja ndi mtunda.


Koma adawakweretsa patsindwi, nawabisa ndi mitengo yanthamza yoyanika patsindwi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa