Danieli 5:6 - Buku Lopatulika6 Pamenepo padasandulika pa nkhope pake pa mfumu, ndi maganizo ake anamsautsa, ndi mfundo za m'chuuno mwake zinaguluka, ndi maondo ake anaombana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pamenepo padasandulika pa nkhope pake pa mfumu, ndi maganizo ake anamsautsa, ndi mfundo za m'chuuno mwake zinaguluka, ndi maondo ake anaombana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Nkhope yake inasandulika ndipo inachita mantha, nkhongono zii, mawondo gwedegwede. Onani mutuwo |