Danieli 4:24 - Buku Lopatulika24 kumasulira kwake ndi uku, mfumu; ndipo chilamuliro cha Wam'mwambamwamba chadzera mbuye wanga mfumu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 kumasulira kwake ndi uku, mfumu; ndipo chilamuliro cha Wam'mwambamwamba chadzera mbuye wanga mfumu: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Tanthauzo lake ndi ili mfumu, izi ndi zimene Mulungu Wammwambamwamba watsimikiza kuti zikugwereni mbuye wanga mfumu: Onani mutuwo |