Danieli 2:42 - Buku Lopatulika42 Ndi zala za mapazi, mwina chitsulo ndi mwina dongo, momwemo ufumuwo, mwina wolimba mwina wogamphuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndi zala za mapazi, mwina chitsulo ndi mwina dongo, momwemo ufumuwo, mwina wolimba mwina wogamphuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Monga zala zinali za chitsulo chosakaniza ndi dongo, choncho ufumu uwu udzakhala pangʼono wolimba ndi pangʼono wofowoka. Onani mutuwo |