Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 2:16 - Buku Lopatulika

16 Nalowa Daniele, nafunsa mfumu amuikire nthawi, kuti aululire mfumu kumasulira kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Nalowa Daniele, nafunsa mfumu amuikire nthawi, kuti aululire mfumu kumasulira kwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Danieli anapita mofulumira kwa mfumu ndipo anamupempha kuti amupatse nthawi kuti amuwuze zimene walota ndi tanthauzo lake.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 2:16
5 Mawu Ofanana  

Mkwiyo wa mfumu ndi mithenga ya imfa; wanzeru adzaukhulula.


anayankha nati kwa Ariyoki mkulu wa olindirira a mfumu, Chilamuliro cha mfumu chifulumiriranji? Pamenepo Ariyoki anadziwitsa Daniele chinthuchi.


Pamenepo Daniele anapita kunyumba kwake, nadziwitsa anzake Hananiya, Misaele, ndi Azariya, chinthuchi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa