Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 2:16 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Danieli anapita mofulumira kwa mfumu ndipo anamupempha kuti amupatse nthawi kuti amuwuze zimene walota ndi tanthauzo lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

16 Nalowa Daniele, nafunsa mfumu amuikire nthawi, kuti aululire mfumu kumasulira kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Nalowa Daniele, nafunsa mfumu amuikire nthawi, kuti aululire mfumu kumasulira kwake.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 2:16
5 Mawu Ofanana  

Ukali wa mfumu ndi mthenga wa imfa, koma munthu wanzeru amawupepesa ukaliwo.


Danieli anafunsa Ariyoki kapitawo wa mfumu kuti, “Chifukwa chiyani mfumu yapereka lamulo lankhanza lotere?” Kenaka Ariyoki anafotokoza nkhaniyi kwa Danieli.


Kenaka Danieli anabwerera ku nyumba kwake ndi kukafotokozera anzake aja zimenezi: Hananiya, Misaeli ndi Azariya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa