Danieli 11:11 - Buku Lopatulika11 Ndi mfumu ya kumwera idzawawidwa mtima, nidzatuluka kulimbana naye, ndiye mfumu ya kumpoto imene idzaonetsa unyinji waukulu; koma unyinjiwo udzaperekedwa m'dzanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndi mfumu ya kumwera adzawawidwa mtima, nadzatuluka kulimbana naye, ndiye mfumu ya kumpoto imene idzaonetsa unyinji waukulu; koma unyinjiwo udzaperekedwa m'dzanja lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Kenaka mfumu yakummwera idzatuluka mokwiya ndi kumenya nkhondo ndi mfumu yakumpoto, imene idzasonkhanitsa gulu lalikulu la nkhondo, koma idzayigonjetsa. Onani mutuwo |