Chivumbulutso 7:3 - Buku Lopatulika3 nanena, Musaipse dziko, kapena nyanja, kapena mitengo, kufikira tidasindikiza chizindikiro akapolo a Mulungu wathu, pamphumi pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nanena, Musaipse dziko, kapena nyanja, kapena mitengo, kufikira tidasindikiza chizindikiro akapolo a Mulungu wathu, pamphumi pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adaŵauza kuti, “Musaononge msanga dziko, kapena nyanja, kapenanso mitengo, tiyambe taŵalemba chizindikiro pa mphumi atumiki a Mulungu wathu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Musawononge dziko, nyanja ndi mitengo kufikira titalemba chizindikiro pa mphumi za atumiki a Mulungu wathu.” Onani mutuwo |
Ndipo ndinaona mipando yachifumu, ndipo anakhala pamenepo; ndipo anawapatsa chiweruziro; ndipo ndinaona mizimu ya iwo amene adawadula khosi chifukwa cha umboni wa Yesu, ndi chifukwa cha mau a Mulungu, ndi iwo amene sanalambire chilombo, kapena fano lake, nisanalandire lembalo pamphumi ndi padzanja lao; ndipo anakhala ndi moyo, nachita ufumu pamodzi ndi Khristu zaka chikwi.