Chivumbulutso 7:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndinaona mngelo wina, anakwera kuchokera potuluka dzuwa, ali nacho chizindikiro cha Mulungu wamoyo: ndipo anafuula ndi mau aakulu kuitana angelo anai, amene adalandira mphamvu kuipsa dziko ndi nyanja, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndinaona mngelo wina, anakwera kuchokera potuluka dzuwa, ali nacho chizindikiro cha Mulungu wamoyo: ndipo anafuula ndi mau akulu kuitana angelo anai, amene adalandira mphamvu kuipsa dziko ndi nyanja, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kenaka ndidaona mngelo wina akukwera kuchokera kuvuma, ali ndi chidindo cha Mulungu wopatsa moyo. Mokweza mau adafuulira angelo anai aja amene Mulungu adaaŵapatsa mphamvu yoonongera dziko ndi nyanja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kenaka ndinaona mngelo wina akuchokera kummawa, ali ndi chidindo cha Mulungu wamoyo. Iye anafuwulira angelo anayi aja amene anapatsidwa mphamvu yowononga dziko ndi nyanja kuti, Onani mutuwo |