Chivumbulutso 2:3 - Buku Lopatulika3 ndipo uli nacho chipiriro, ndipo walola chifukwa cha dzina langa, wosalema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndipo uli nacho chipiriro, ndipo walola chifukwa cha dzina langa, wosalema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndinudi opirira kolimba, ndipo mwasauka kwambiri chifukwa cha Ine, osatopa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iwe wapirira ndipo wakumana ndi zovuta chifukwa cha dzina langa, ndipo sunatope. Onani mutuwo |