Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Chivumbulutso 2:4 - Buku Lopatulika

4 Koma ndili nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya chikondi chako choyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma ndili nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya chikondi chako choyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Komatu pokudzudzulirani palipo: ndi apa pakuti mwasiya chikondi chimene munkandikonda nacho poyamba paja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Komabe ndili ndi chotsutsana nawe: Wataya chikondi chako chapoyamba.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 2:4
11 Mawu Ofanana  

Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao.


Ndipo ichi ndipempha, kuti chikondi chanu chisefukire chionjezere, m'chidziwitso, ndi kuzindikira konse;


Tiziyamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu, abale, monga kuyenera; pakuti chikhulupiriro chanu chikula chikulire, ndipo chichulukira chikondano cha inu nonse, yense pa mnzake;


Komatu ndili nazo zinthu pang'ono zotsutsana ndi iwe, popeza uli nao komweko akugwira chiphunzitso cha Balamu, amene anaphunzitsa Balaki aponye chokhumudwitsa pamaso pa ana a Israele, kuti adye zoperekedwa nsembe kwa mafano, nachite chigololo.


Komatu ndili nako kotsutsana ndi iwe, kuti ulola mkazi Yezebele, wodzitcha yekha mneneri; ndipo aphunzitsa, nasocheretsa akapolo anga, kuti achite chigololo ndi kudya zoperekedwa nsembe kwa mafano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa