Chivumbulutso 2:4 - Buku Lopatulika4 Koma ndili nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya chikondi chako choyamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma ndili nako kanthu kotsutsana ndi iwe, kuti unataya chikondi chako choyamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Komatu pokudzudzulirani palipo: ndi apa pakuti mwasiya chikondi chimene munkandikonda nacho poyamba paja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Komabe ndili ndi chotsutsana nawe: Wataya chikondi chako chapoyamba. Onani mutuwo |