Chivumbulutso 10:3 - Buku Lopatulika3 nafuula ndi mau aakulu, monga ngati mkango ubangula; ndipo pamene anafuula mabingu asanu ndi awiri analankhula mau ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nafuula ndi mau akulu, monga ngati mkango ubangula; ndipo pamene anafuula mabingu asanu ndi awiri analankhula mau ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono adaafuula mokweza ngati kubangula kwa mkango. Mngeloyo atangofuula choncho, mabingu asanu ndi aŵiri aja adagunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mngeloyo anafuwula kwambiri ngati kubangula kwa mkango. Atangofuwula, kunamveka kugunda kwa mabingu asanu ndi awiri. Onani mutuwo |