Amosi 9:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti taonani, ndidzalamulira, ndipo ndidzapeta nyumba ya Israele mwa amitundu onse, monga apeta tirigu m'lichero; koma silidzagwa pansi diso, ndi limodzi lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti taonani, ndidzalamulira, ndipo ndidzapeta nyumba ya Israele mwa amitundu onse, monga apeta tirigu m'lichero; koma silidzagwa pansi diso, ndi limodzi lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Ai, ndidzalamula, ndipo ndidzagwedeza Aisraele uku ndi uku pakati pa mitundu yonse ya anthu monga momwe amagwedezera sefa uku ndi uku, popanda kamwala nkamodzi komwe kogwa pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Pakuti ndidzalamula, ndipo ndidzagwedeza nyumba ya Israeli pakati pa mitundu yonse ya anthu monga momwe amasefera ufa mʼsefa, koma palibe nʼkamwala kamodzi komwe kamene kadzagwe pansi. Onani mutuwo |