Amosi 9:10 - Buku Lopatulika10 Ochimwa onse a anthu anga adzafa ndi lupanga, ndiwo amene akuti, Choipa sichidzatipeza, kapena kutidulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ochimwa onse a anthu anga adzafa ndi lupanga, ndiwo amene akuti, Choipa sichidzatipeza, kapena kutidulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adzafera pa nkhondo anthu anga onse ochimwa, iwo amene amati, ‘Chilango sichidzatifika, kapena kutipambana.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anthu onse ochimwa pakati pa anthu anga adzaphedwa ndi lupanga, onse amene amanena kuti, ‘Tsoka silidzatigwera ife kapena kutiwononga.’ Onani mutuwo |