Amosi 9:8 - Buku Lopatulika8 Taonani, maso a Ambuye Yehova ali pa ufumu wochimwawo, ndipo ndidzauononga kuuchotsa padziko lapansi; pokhapo sindidzaononga nyumba ya Yakobo kuitha konse, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Taonani, maso a Ambuye Yehova ali pa ufumu wochimwawo, ndipo ndidzauononga kuuchotsa pa dziko lapansi; pokhapo sindidzaononga nyumba ya Yakobo kuitha konse, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ine, Ambuye Chauta, maso anga ali pa dziko lochimwalo, ndipo ndidzalifafaniza pa dziko lapansi. Komabe banja la Yakobe lokha sindidzaliwononga kotheratu.” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Taonani, maso a Ambuye Yehova ali pa ufumu wochimwawu. Ndidzawufafaniza pa dziko lapansi. Komabe sindidzawononga kotheratu nyumba ya Yakobo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |