Amosi 9:7 - Buku Lopatulika7 Kodi simukhala kwa Ine ngati ana a Kusi, inu ana a Israele? Ati Yehova. Sindinakweza Israele ndine, kumtulutsa m'dziko la Ejipito, ndi Afilisti ku Kafitori, ndi Aaramu ku Kiri? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kodi simukhala kwa Ine ngati ana a Kusi, inu ana a Israele? Ati Yehova. Sindinakweza Israele ndine, kumtulutsa m'dziko la Ejipito, ndi Afilisti ku Kafitori, ndi Aaramu ku Kiri? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Kwa Ine, Aisraelenu muli ngati Aetiopiya.” Akuterotu Chauta. “Kodi sindine uja ndidatulutsa Aisraele ku Ejipito? Kodi sindine uja ndidatulutsa Afilisti ku Kafitori ndi Asiriya ku Kiri? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Kodi kwa Ine, inu Aisraeli, simuli chimodzimodzi ndi Akusi?” Akutero Yehova. “Kodi sindine amene ndinatulutsa Israeli ku Igupto, Afilisti ku Kafitori ndi Aaramu ku Kiri? Onani mutuwo |