Amosi 8:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ati Ambuye Yehova, ndidzalowetsa dzuwa usana, ndi kudetsa dziko pausana poyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ati Ambuye Yehova, ndidzalowetsa dzuwa usana, ndi kudetsa dziko pausana poyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ambuye Chauta akunena kuti, “Pa tsiku limenelo ndidzadetsa dzuŵa masana, ndidzagwetsa mdima pa dziko lapansi dzuŵa lili nye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akunena kuti, “Ndidzadetsa dzuwa masana ndi kugwetsa mdima pa dziko lapansi dzuwa likuswa mtengo. Onani mutuwo |