Amosi 8:3 - Buku Lopatulika3 Koma nyimbo za ku Kachisi zidzasanduka kubuma tsiku ilo, ati Ambuye Yehova; mitembo idzachuluka; adzaitaya paliponse padzakhala zii. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma nyimbo za ku Kachisi zidzasanduka kubuma tsiku ilo, ati Ambuye Yehova; mitembo idzachuluka; adzaitaya paliponse padzakhala zii. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nyimbo za m'Nyumba ya Mulungu zidzasanduka kulira pa tsiku limenelo. Mitembo ya anthu idzachuluka, ndipo adzaiponya ponseponse. Kudzangoti zii!” Akuterotu Ambuye Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akulengeza kuti, “Nyimbo za mʼNyumba ya Mulungu zidzasanduka kulira kofuwula. Mitembo ya anthu idzachuluka, ndipo adzayiponya ponseponse! Kudzangoti zii!” Onani mutuwo |