Amosi 8:4 - Buku Lopatulika4 Tamverani ichi, inu akumeza aumphawi, ndi kuwatha ofatsa m'dziko, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tamverani ichi, inu akumeza aumphawi, ndi kuwatha ofatsa m'dziko, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amosi adati, “Imvani izi, inu amene mumapondereza osoŵa, amene mufuna kuwononga anthu osauka am'dzikomu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Imvani izi, inu amene mumapondereza anthu osowa ndipo simulabadira anthu osauka a mʼdzikomu. Onani mutuwo |