Amosi 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anati, Amosi uona chiyani? Ndipo ndinati, Dengu la zipatso zamalimwe. Nati Yehova kwa ine, Chitsiriziro chafikira anthu anga Israele, sindidzawalekanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anati, Amosi uona chiyani? Ndipo ndinati, Dengu la zipatso zamalimwe. Nati Yehova kwa ine, Chitsiriziro chafikira anthu anga Israele, sindidzawalekanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta adandifunsa kuti, “Kodi iwe Amosi, nchiyani ukuwonachi?” Ine ndidayankha kuti, “Dengu la zipatso zakupsa.” Tsono Chauta adandiwuza kuti, “Nthaŵi ya chimalizo yaŵakwanira anthu anga Aisraele, sindidzaŵakhululukiranso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anandifunsa kuti, “Amosi nʼchiyani ukuona?” Ine ndinayankha kuti, “Dengu la zipatso zakupsa.” Ndipo Yehova anati kwa ine, “Nthawi yachimaliziro yawakwanira anthu anga Aisraeli; sindidzawakhululukiranso. Onani mutuwo |