Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Amosi 8:1 - Buku Lopatulika

1 Ambuye Yehova anandionetsa chotere; ndipo taonani, dengu la zipatso zamalimwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ambuye Yehova anandionetsa chotere; ndipo taonani, dengu la zipatso zamalimwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Zinanso zimene Ambuye Chauta adandiwonetsa m'masomphenya ndi izi: Panali dengu la zipatso zakupsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Zimene Ambuye Yehova anandionetsa ndi izi: dengu la zipatso zakupsa.

Onani mutuwo Koperani




Amosi 8:1
6 Mawu Ofanana  

Yehova anandionetsa ine, ndipo, taonani, madengu awiri a nkhuyu oikidwa pakhomo pa Kachisi wa Yehova; Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni atachotsa am'nsinga Yekoniya mwana wake wa Yehoyakimu, mfumu ya Yuda, ndi akulu a Yuda, ndi amisiri ndi achipala, kuwachotsa ku Yerusalemu, nawatengera ku Babiloni.


Ambuye Yehova anandionetsa chotere; ndipo taonani, anaumba dzombe, poyamba kuphuka kwa udzu wa chibwereza; ndipo taonani, ndicho chibwereza atawusengera mfumu.


chifukwa chake atero Yehova, Mkazi wako adzakhala wadama m'mzinda, ndi ana ako aamuna ndi aakazi adzagwa ndi lupanga, ndi dziko lako lidzagawanidwa ndi kuyesa chingwe, ndi iwe mwini udzafa m'dziko lodetsedwa; ndipo Israele adzatengedwadi ndende kuchoka m'dziko lake.


Ambuye Yehova anandionetsa chotere; ndipo taonani, Ambuye Yehova anaitana kuti atsutse ndi moto; ndipo unanyambita chakuya chachikulu ukadanyambitanso dziko.


Anandionetsa chotere; ndipo taonani, Ambuye anaima pa khoma lomangidwa ndi chingwe cholungamitsira chilili; ndi chingwe cholungamitsira chilili m'dzanja lake.


Ndipo anati, Amosi uona chiyani? Ndipo ndinati, Dengu la zipatso zamalimwe. Nati Yehova kwa ine, Chitsiriziro chafikira anthu anga Israele, sindidzawalekanso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa