Amosi 7:9 - Buku Lopatulika9 ndi misanje ya Isaki idzakhala bwinja; ndi malo opatulika a Israele adzapasuka; ndipo ndidzaukira nyumba ya Yerobowamu ndi lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 ndi misanje ya Isaki idzakhala bwinja; ndi malo opatulika a Israele adzapasuka; ndipo ndidzaukira nyumba ya Yerobowamu ndi lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Akachisi a ana a Isaki adzasanduka bwinja, malo achipembedzo a Aisraele adzaonongedwa. Ndipo ndidzagwetsa banja la mfumu Yerobowamu pa nkhondo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Malo achipembedzo a Isake adzawonongedwa ndipo malo opatulika a Israeli adzasanduka bwinja; ndidzagwetsa nyumba ya Yeroboamu ndi lupanga langa.” Onani mutuwo |