Amosi 7:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Yehova anati kwa ine, Amosi, uona chiyani? Ndipo ndinati, Chingwe cholungamitsira chilili. Nati Ambuye, Taona, ndidzaika chingwe cholungamitsira chilili pakati pa anthu anga Israele, sindidzawalekanso: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Yehova anati kwa ine, Amosi, uona chiyani? Ndipo ndinati, Chingwe cholungamitsira chilili. Nati Ambuye, Taona, ndidzaika chingwe cholungamitsira chilili pakati pa anthu anga Israele, sindidzawalekanso: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono Chautayo adandifunsa kuti, “Kodi iwe Amosi, nchiyani ukuwonachi?” Ine ndidayankha kuti, “Chingwe choongolera khoma.” Apo Chauta adati, “Ndikuika chingwe chimenechi pakati pa anthu anga Aisraele kuti kuwoneke kukhota kwao, choncho sindidzaŵalekereranso ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo Ambuye anandifunsa kuti, “Amosi, nʼchiyani ukuonachi?” Ine ndinayankha kuti, “Chingwe chowongolera khoma.” Ndipo Yehova anati, “Taona, Ine ndikuyika chingwe chowongolerachi pakati pa anthu anga, Aisraeli; sindidzawalekereranso. Onani mutuwo |