Amosi 7:7 - Buku Lopatulika7 Anandionetsa chotere; ndipo taonani, Ambuye anaima pa khoma lomangidwa ndi chingwe cholungamitsira chilili; ndi chingwe cholungamitsira chilili m'dzanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Anandionetsa chotere; ndipo taonani, Ambuye anaima pa khoma lomangidwa ndi chingwe cholungamitsira chilili; ndi chingwe cholungamitsira chilili m'dzanja lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Zina ndi izi zimene Chauta adandiwonetsa m'masomphenya: Ndidaona Iye ataima pamwamba pa khoma lomangamanga, m'manja mwake ali ndi chingwe choongolera khoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Zimene Iye anandionetsa ndi izi: Ambuye anayima pambali pa khoma lomangamanga, mʼmanja mwake muli chingwe chowongolera khoma. Onani mutuwo |