Amosi 7:14 - Buku Lopatulika14 Pamenepo Amosi anayankha, nati kwa Amaziya, Sindinali mneneri, kapena mwana wa mneneri, koma ndinali woweta ng'ombe, ndi wakutchera nkhuyu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamenepo Amosi anayankha, nati kwa Amaziya, Sindinali mneneri, kapena mwana wa mneneri, koma ndinali woweta ng'ombe, ndi wakutchera nkhuyu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Amosi adayankha Amaziya kuti, “Ine sindine mneneri konse, kapenanso wa m'gulu la aneneri. Inetu ndine woŵeta nkhosa, ndiponso wolima nkhuyu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Amosi anayankha Amaziya kuti, “Ine sindine mneneri kapena mwana wa mneneri; koma ndine woweta ziweto, ndiponso mlimi wa nkhuyu. Onani mutuwo |