Amosi 7:15 - Buku Lopatulika15 ndipo Yehova ananditenga ndilikutsata nkhosa, nati kwa ine Yehova, Muka, nenera kwa anthu anga Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 ndipo Yehova ananditenga ndilikutsata nkhosa, nati kwa ine Yehova, Muka, nenera kwa anthu anga Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chauta adachita kukanditenga, kundileketsa ntchito yoŵeta nkhosa, nandiwuza kuti, ‘Pita, ukalalikire anthu anga, Aisraele.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma Yehova ananditenga ndikuweta nkhosa ndipo anati, ‘Pita ukanenere kwa anthu anga Aisraeli.’ Onani mutuwo |