Amosi 7:13 - Buku Lopatulika13 koma usaneneranso ku Betele; pakuti pamenepo mpamalo opatulika a mfumu, ndiyo nyumba yachifumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 koma usaneneranso ku Betele; pakuti pamenepo mpa malo opatulika a mfumu, ndiyo nyumba yachifumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma usakalosenso ku Betele poti kumeneko ndi malo opatulika a mfumu, ndiponso ndi Nyumba ya Mulungu ya m'dziko lino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Usanenerenso ku Beteli, chifukwa kumeneko ndi malo opatulika a mfumu ndiponso ndi malo a nyumba yachipembedzo yaufumu.” Onani mutuwo |