Amosi 7:12 - Buku Lopatulika12 Amaziya anatinso kwa Amosi, Mlauli iwe, choka, thawira kudziko la Yuda, nudye, nunenere komweko; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Amaziya anatinso kwa Amosi, Mlauli iwe, choka, thawira kudziko la Yuda, nudye, nunenere komweko; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono Amaziya adauza Amosi kuti, “Mlosi iwe, choka kuno! Thaŵira ku dziko la Yuda! Uzikalosa kumeneko, ndipo anthu akumeneko azikakudyetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo Amaziya anawuza Amosi kuti, “Choka, mlosi iwe! Bwerera ku dziko la Yuda. Uzikalosera kumeneko ndipo anthu a kumeneko azikakudyetsa. Onani mutuwo |