Amosi 7:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti atero Amosi, Yerobowamu adzafa ndi lupanga, ndi Israele adzatengedwadi ndende, kuchoka m'dziko lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti atero Amosi, Yerobowamu adzafa ndi lupanga, ndi Israele adzatengedwadi ndende, kuchoka m'dziko lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Amosiyo akunena kuti, ‘Yerobowamu adzafa pa nkhondo, ndipo Aisraele adzatengedwa kunka ku ukapolo, kutali ndi dziko lao.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti zimene Amosi akunena ndi izi: “ ‘Yeroboamu adzaphedwa ndi lupanga, ndipo Israeli adzapita ndithu ku ukapolo, kutali ndi dziko lake.’ ” Onani mutuwo |