Amosi 6:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kudzachitika, mukatsala amuna khumi m'nyumba imodzi, adzafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kudzachitika, mukatsala amuna khumi m'nyumba imodzi, adzafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Anthu khumi akadzakhala akubisala m'nyumba imodzi, nawonso adzafabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ngati anthu khumi otsala adzabisala mʼnyumba imodzi, nawonso adzafa ndithu. Onani mutuwo |