Amosi 6:8 - Buku Lopatulika8 Ambuye Yehova walumbira pali Iye mwini, ati Yehova Mulungu wa makamu, Ndinyansidwa nako kudzikuza kwa Yakobo, ndidana nazo nyumba zake zachifumu; m'mwemo ndidzapereka mzinda, ndi zonse zili m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ambuye Yehova walumbira pali Iye mwini, ati Yehova Mulungu wa makamu, Ndinyansidwa nako kudzikuza kwa Yakobo, ndidana nazo nyumba zake zachifumu; m'mwemo ndidzapereka mudzi, ndi zonse zili m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ambuye Chauta alumbira m'dzina lao kuti, “Ndikunyansidwa ndi zimene ana a Yakobe akunyadira, ndikudana nazo nyumba zao zazikulu. Ndithu ndidzapereka kwa adani ao likulu lao ndi zonse zam'menemo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ambuye Yehova walumbira mʼdzina lake. Yehova Mulungu Wamphamvuzonse walengeza kuti, “Ndimanyansidwa ndi kunyada kwa Yakobo, ndimadana ndi nyumba zake zaufumu; Ine ndidzawupereka mzindawu pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo.” Onani mutuwo |