Amosi 6:7 - Buku Lopatulika7 Chifukwa chake tsono, adzatengedwa ndende ndi oyamba kutengedwa ndende; ndi phokoso la iwo odzithinula lidzapita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chifukwa chake tsono, adzatengedwa ndende ndi oyamba kutengedwa ndende; ndi phokoso la iwo odzithinula lidzapita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake mudzatsogola ndinu kupita ku ukapolo, ndipo maphwando ndi zikondwerero zidzakutherani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nʼchifukwa chake inu mudzakhala mʼgulu la anthu oyamba kupita ku ukapolo; maphwando ndi zikondwerero zanu zidzatheratu. Onani mutuwo |