Amosi 6:6 - Buku Lopatulika6 akumwera vinyo m'zipanda, nadzidzoza ndi mafuta abwino oposa, osagwidwa chisoni ndi kuthyoka kwa Yosefe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 akumwera vinyo m'zipanda, nadzidzoza ndi mafuta abwino oposa, osagwidwa chisoni ndi kuthyoka kwa Yosefe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsoka kwa inu amene mumamwera vinyo m'zipanda zodzaza, inu amene mumadzola mafuta abwino kwambiri, koma simumva chisoni ndi kuwonongeka kwa dziko la Yosefe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mumamwera vinyo mʼzipanda zodzaza ndipo mumadzola mafuta abwino kwambiri, koma simumva chisoni ndi kuwonongeka kwa Yosefe. Onani mutuwo |