Amosi 6:5 - Buku Lopatulika5 akungoimba kutsata maliridwe a zeze, nadzilingiririra zoimbira nazo ngati Davide; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 akungoimba kutsata maliridwe a zeze, nadzilingiririra zoimbira nazo ngati Davide; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ntchito nkumangoimba azeze ngati Davide, ndi kumangopeka nyimbo zoimbira pa zing'wenyeng'wenye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mumayimba azeze anu ndi kumangopeka nyimbo pa zingʼwenyengʼwenye ngati Davide. Onani mutuwo |