Amosi 6:4 - Buku Lopatulika4 ogona pamakama aminyanga, nadzithinula pa maguwa ao ogonapo, nadya anaankhosa a kuzoweta, ndi anaang'ombe ochoka pakati pa khola; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ogona pamakama aminyanga, nadzithinula pa maguwa ao ogonapo, nadya anaankhosa a kuzoweta, ndi anaang'ombe ochoka pakati pa khola; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsoka kwa inu amene mumagona pa mabedi oŵakongoletsa ndi minyanga yanjovu, inu amene mumangoti lamzi pa mipando yanu, nkumachita phwando la nyama ya anaankhosa osakhwima ndi ya anaang'ombe onenepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mumagona pa mabedi owakongoletsa ndi minyanga ya njovu, mumagona pa mipando yanu ya wofuwofu. Mumadya ana ankhosa onona ndi ana angʼombe onenepa. Onani mutuwo |