Amosi 5:9 - Buku Lopatulika9 wakufikitsa chionongeko pa wamphamvu modzidzimuka, kuti chionongekocho chigwere linga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 wakufikitsa chionongeko pa wamphamvu modzidzimuka, chionongeko nichigwera linga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndiyenso amene amakantha olamulira ankhanza, ndiye amene amagumula malinga ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu ndi kuwononga mizinda yotetezedwa), Onani mutuwo |