Amosi 5:2 - Buku Lopatulika2 Namwali wa Israele wagwa, sadzaukanso; wagwetsedwa pa nthaka yake, palibe womuutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Namwali wa Israele wagwa, sadzaukanso; wagwetsedwa pa nthaka yake, palibe womuutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Namwali Israele wagwa chonse osati nkudzukanso ai. Wagwa ndi kuiŵalika pa dziko lake, popanda wina womdzutsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Namwali Israeli wagwa, moti sadzadzukanso, wasiyidwa mʼdziko lake lomwe, popanda woti ndi kumudzutsa.” Onani mutuwo |