Amosi 5:1 - Buku Lopatulika1 Tamverani mau awa ndinenawa, akhalire inu nyimbo ya maliro, nyumba ya Israele inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tamverani mau awa ndinenawa, akhalire inu nyimbo ya maliro, nyumba ya Israele inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu banja la Israele imvani mau aŵa, amene ndikukuuzani mwadandaulo: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo: Onani mutuwo |