Amosi 4:5 - Buku Lopatulika5 nimutenthe nsembe zolemekeza zachotupitsa, nimulalikire nsembe zaufulu, ndi kuzimveketsa; pakuti ichi muchikonda, inu ana a Israele, ati Ambuye Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 nimutenthe nsembe zolemekeza zachotupitsa, nimulalikire nsembe zaufulu, ndi kuzimveketsa; pakuti ichi muchikonda, inu ana a Israele, ati Ambuye Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mupereke buledi wanu kuti muthokoze Mulungu. Munene poyera ndi kulengeza zopereka zanu zaufulu, pakuti nzimene mumakonda kuchita, inu Aisraele.” Akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Wotchani buledi wokhala ndi yisiti ngati nsembe yachiyamiko ndi kumanyadira poyera za zopereka zanu zaufulu. Inu Aisraeli, zinyadireni nsembezo, pakuti izi ndi zimene mumakonda kuchita,” akutero Ambuye Yehova. Onani mutuwo |