Amosi 4:4 - Buku Lopatulika4 Idzani ku Betele, mudzalakwe ku Giligala, nimuchulukitse zolakwa, nimubwere nazo nsembe zanu zophera m'mawa ndi m'mawa, magawo anu akhumi atapita masiku atatuatatu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Idzani ku Betele, mudzalakwe ku Giligala, nimuchulukitse zolakwa, nimubwere nazo nsembe zanu zophera m'mawa ndi m'mawa, magawo anu akhumi atapita masiku atatuatatu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Bwerani ku malo oyera ku Betele, mudzachimwireko. Bweranazoni nsembe zanu m'maŵa mulimonse, bweranazoni zopereka zanu zachikhumi pa masiku atatu aliwonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Bwerani ku Beteli mudzachimwe; ndi ku Giligala kuti mudzapitirize kuchimwa. Bweretsani nsembe zanu mmawa uliwonse, bweretsani chakhumi chanu masiku atatu aliwonse. Onani mutuwo |