Amosi 4:11 - Buku Lopatulika11 Ndinagubuduza ena mwa inu, monga umo Mulungu anagubuduzira Sodomu ndi Gomora; ndipo inu munali ngati muuni wofumulidwa kumoto; koma simunabwerere kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndinagubuduza ena mwa inu, monga umo Mulungu anagubuduzira Sodomu ndi Gomora; ndipo inu munali ngati muuni wofumulidwa kumoto; koma simunabwerera kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Ndidaononga ena mwa inu, monga momwe ndidaonongera Sodomu ndi Gomora. Otsaliranu munali ngati zikuni zofumula pa moto. Komabe simudabwerere kwa Ine.” Akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Ndinawononga ena mwa inu monga ndinawonongera Sodomu ndi Gomora. Inu munali ngati chikuni choyaka chimene chafumulidwa pa moto. Komabe inu simunabwerere kwa Ine,” akutero Yehova. Onani mutuwo |