Amosi 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndinatumiza mliri pakati panu monga mu Ejipito; anyamata anu ndawapha ndi lupanga, ndi kutenga akavalo anu; ndipo ndinakweretsa kununkha kwa chigono chanu kufikitsa kumphuno kwanu; koma simunabwerere kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndinatumiza mliri pakati panu monga m'Ejipito; anyamata anu ndawapha ndi lupanga, ndi kutenga akavalo anu; ndipo ndinakweretsa kununkha kwa chigono chanu kufikitsa kumphuno kwanu; koma simunabwerera kudza kwa Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Ndidakugwetserani miliri yonga ya ku Ejipito ija. Ndidaphetsa achinyamata anu ku nkhondo, ndidapereka akavalo anu kwa adani. Ndidakununkhitsani fungo la mitembo lochokera ku misasa yanu yankhondo. Komabe simudabwerere kwa Ine.” Akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Ine ndinabweretsa miliri pakati panu monga ndinachitira ku Igupto. Ndinapha anyamata anu ndi lupanga, ndinapereka akavalo anu kwa adani. Ndinakununkhitsani fungo la mitembo lochokera mʼmisasa yanu ya nkhondo. Komatu inu simunabwerere kwa Ine,” akutero Yehova. Onani mutuwo |